Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 2:8 - Buku Lopatulika

Ndipo nanga ife timva bwanji, yense m'chilankhulidwe chathu chimene tinabadwa nacho?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo nanga ife timva bwanji, yense m'chilankhulidwe chathu chimene tinabadwa nacho?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nanga bwanji aliyense mwa ife akuŵamva akulankhula chilankhulo chakwao?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nanga bwanji aliyense wa ife akuwamva iwo mu chinenero cha kwawo?

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 2:8
5 Mawu Ofanana  

Kudziwitsa ana a anthu zamphamvu zake, ndi ulemerero waukulu wa ufumu wake.


Ndipo atate wake Zekariya anadzazidwa ndi Mzimu Woyera, nanenera za Mulungu, nati,


Ndipo anadabwa onse, nazizwa, nanena, Taonani, awa onse alankhulawa sali Agalileya kodi?


Aparti ndi Amedi, ndi Aelamu, ndi iwo akukhala mu Mesopotamiya, mu Yudeya, ndiponso mu Kapadokiya, mu Ponto, ndi mu Asiya;


Ndipotu Mulungu anaika ena mu Mpingo, poyamba atumwi, achiwiri aneneri, achitatu aphunzitsi, pamenepo zozizwa, pomwepo mphatso za machiritso, mathandizo, maweruziro, malilime a mitundumitundu.