Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 2:16 - Buku Lopatulika

komatu ichi ndi chimene chinanenedwa ndi mneneri Yowele,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

komatu ichi ndi chimene chinanenedwa ndi mneneri Yowele,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma zimenezi ndi zomwe mneneri Yowele adalosa kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma izi ndi zimene ananena Mneneri Yoweli kuti:

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 2:16
5 Mawu Ofanana  

Mau a Yehova a kwa Yowele mwana wa Petuwele.


Ndipo kudzachitika tsiku lomwelo, sikudzakhala kuunika, zowalazo zidzada;


Pakuti awa sanaledzere monga muyesa inu; pakuti ndi ora lachitatu lokha la tsiku;


Ndipo kudzali m'masiku otsiriza, anena Mulungu, ndidzathira cha Mzimu wanga pa thupi lililonse, ndipo ana anu aamuna, ndi aakazi adzanenera, ndipo anyamata anu adzaona masomphenya, ndi akulu anu adzalota maloto;