Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 17:9 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene analandira chikole kwa Yasoni ndi enawo, anawamasula.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene analandira chikole kwa Yasoni ndi enawo, anawamasula.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Yasoni ndi anzake aja atalipira mlanduwo, akuluwo adaŵamasula.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo analipiritsa Yasoni ndi anzakewo ndipo anawamasula.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 17:9
2 Mawu Ofanana  

Koma Ayuda anadukidwa mtima, natenga anthu ena oipa achabe a pabwalo, nasonkhanitsa khamu la anthu, nachititsa phokoso m'mzinda; ndipo anagumukira kunyumba ya Yasoni, nafuna kuwatulutsira kwa anthu.


Ndipo anavuta anthu, ndi akulu a mzinda, pamene anamva zimenezi.