Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 17:8 - Buku Lopatulika

Ndipo anavuta anthu, ndi akulu a mzinda, pamene anamva zimenezi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anavuta anthu, ndi akulu a mudzi, pamene anamva zimenezi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mau ameneŵa adautsa mitima ya anthuwo ndi ya akulu amumzinda aja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atamva zimenezi, gulu la anthu ndi akulu a mzinda anavutika mu mtima.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 17:8
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Herode mfumuyo pakumva ichi anavutika, ndi Yerusalemu yense pamodzi naye.


Ndipo pamene paliponse adzamuka nanu kumlandu wa m'sunagoge ndi kwa akulu, ndi aulamuliro, musade nkhawa ndi kuti mukadzikanira bwanji, ndipo ndi mau otani, kapena mukanena chiyani;


Ngati timleka Iye kotero, onse adzakhulupirira Iye; ndipo adzadza Aroma nadzachotsa malo athu ndi mtundu wathu.


amene Yasoni walandira; ndipo onsewo achita zokana malamulo a Kaisara; nanena kuti pali mfumu ina, Yesu.


Ndipo pamene analandira chikole kwa Yasoni ndi enawo, anawamasula.