Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 11:7 - Buku Lopatulika

Ndipo ndinamvanso mau akunena ndi ine, Tauka Petro; ipha, nudye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndinamvanso mau akunena ndi ine, Tauka Petro; ipha, nudye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ndidamva mau ondiwuza kuti, ‘Petro dzuka, ipha, udye.’

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka ine ndinamva mawu akuti, ‘Petro, Imirira. Ipha, nudye.’

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 11:7
3 Mawu Ofanana  

chimenecho ndidachipenyetsetsa ndinachilingirira, ndipo ndinaona nyama za miyendo inai za padziko ndi zilombo, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga.


Koma ndinati, Iaitu, Ambuye; pakuti kanthu wamba, kapena konyansa sikanalowe m'kamwa mwanga ndi kale lonse.


Pakuti cholengedwa chonse cha Mulungu nchabwino, ndipo palibe kanthu kayenera kutayika, ngati kalandiridwa ndi chiyamiko;