Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 11:4 - Buku Lopatulika

Koma Petro anayamba kuwafotokozera chilongosolere, nanena,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Petro anayamba kuwafotokozera chilongosolere, nanena,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Petro adayamba kuŵafotokozera mwatsatanetsatane zimene zidachitika. Adati,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Petro anayamba kuwafotokozera zonse mwatsatanetsatane momwe zinachitikira kuti,

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 11:4
5 Mawu Ofanana  

Mayankhidwe ofatsa abweza mkwiyo; koma mau owawitsa aputa msunamo.


ndipo sanalankhule nao wopanda fanizo: koma m'tseri anatanthauzira zonse kwa ophunzira ake.


kuyambira pachiyambi, ndinayesa nkokoma inenso, amene ndinalondalonda mosamalitsa zinthu zonse kuyambira pachiyambi, kulembera kwa iwe tsatanetsatane, Teofilo wabwinotu iwe;


Pamene anafika nasonkhanitsa Mpingo anabwerezanso zomwe Mulungu anachita nao, kuti anatsegulira amitundu pa khomo la chikhulupiriro.