Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 9:8 - Buku Lopatulika

koma ena, kuti Eliya anaoneka; ndipo ena, kuti mneneri wina wa akale aja anauka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma ena, kuti Eliya anaoneka; ndipo ena, kuti mneneri wina wa akale aja anauka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ena ankanena kuti, “Iyai, ameneyu ndi Eliya, waonekanso.” Enanso ankati, “Iyai, koma ndi mmodzi mwa aneneri akale aja, wauka kwa akufa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ena amati Eliya waonekera, ndipo ena anatinso mmodzi wa aneneri akalekale waukanso.

Onani mutuwo



Luka 9:8
6 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anati, Ena ati, Yohane Mbatizi; koma ena, Eliya; ndipo enanso Yeremiya, kapena mmodzi wa aneneri.


Ndipo ophunzira ake anamfunsa, nanena, Ndipo bwanji alembi amanena kuti Eliya ndiye atsogole kudza?


Koma ena ananena, kuti, Ndiye Eliya. Anati enanso, Ndiye mneneri, monga ngati mmodzi wa aneneriwo.


Ndipo ananena, nati, Yohane Mbatizi; ndi ena, Eliya; koma ena, Mmodzi wa aneneri.


Ndipo anayankha nati, Yohane Mbatizi; koma ena, Eliya; ndi ena, kuti anauka mmodzi wa aneneri akale.


Ndipo anamfunsa iye, Nanga bwanji? Ndiwe Eliya kodi? Nanena iye, Sindine iye. Ndiwe Mneneriyo kodi? Nayankha, Iai.