Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 9:53 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo sanamlandire Iye, chifukwa nkhope yake inali yoloza kunka ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo sanamlandire Iye, chifukwa nkhope yake inali yoloza kunka ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma anthu am'mudzimo sadafune kumlandira, chifukwa Iye ankapita ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

koma anthu kumeneko sanamulandire chifukwa Iye ankapita ku Yerusalemu.

Onani mutuwo



Luka 9:53
4 Mawu Ofanana  

Amene aliyense akalandire kamwana aka m'dzina langa alandira Ine; ndipo amene andilandira Ine alandira Iye amene anandituma Ine; pakuti iye wakukhala wamng'onong'ono wa inu nonse, yemweyu ndiye wamkulu.


Makolo athu analambira m'phiri ili; ndipo inu munena, kuti mu Yerusalemu muli malo oyenera kulambiramo anthu.


Pamenepo mkazi wa mu Samariya ananena ndi Iye, Bwanji Inu, muli Myuda, mupempha kwa ine kumwa, ndine mkazi Msamariya? (Pakuti Ayuda sayenderana nao Asamariya).