Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 9:21 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye anawauzitsa iwo, nalamulira kuti asanene ichi kwa munthu aliyense;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye anawauzitsa iwo, nalamulira kuti asanene ichi kwa munthu aliyense;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adalamula ophunzira ake kuti asauze munthu wina aliyense zimenezi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anawachenjeza kwambiri kuti asawuze wina aliyense za izi.

Onani mutuwo



Luka 9:21
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo analamulira ophunzira kuti asauze munthu kuti Iye ndiye Khristu.


Ndipo pamene anali kutsika paphiri, Yesu anawalamula iwo kuti, Musakauze munthu choonekacho, kufikira Mwana wa Munthu adadzauka kwa akufa.


Ndipo Yesu ananena naye, Ona, iwe, usauze munthu; koma muka, udzionetse wekha kwa wansembe, nupereke mtulo umene anaulamulira Mose, ukhale mboni kwa iwo.


Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.