Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 9:17 - Buku Lopatulika

Ndipo anadya, nakhuta onsewo; natola makombo, madengu khumi ndi awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anadya, nakhuta onsewo; natola makombo, madengu khumi ndi awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu onse aja adadya nakhuta. Ndipo ophunzira aja adatola zotsala, nkudzaza madengu khumi ndi aŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Onse anadya nakhuta, ndipo ophunzira ake anatolera madengu khumi ndi awiri odzaza ndi nyenyeswa zomwe zinatsala.

Onani mutuwo



Luka 9:17
13 Mawu Ofanana  

Potero anawagawira, nadya, nasiyapo, monga mwa mau a Yehova.


Pakuti akhutitsa mtima wolakalaka, nadzaza mtima wanjala ndi zabwino.


Zochepa zake za wolungama zikoma koposa kuchuluka kwao kwa oipa ambiri.


Wolungama adya nakhutitsa moyo wake; koma mimba ya oipa idzasowa.


Ndipo Iye, m'mene anatenga mikate isanu ija ndi nsomba ziwiri anayang'ana kumwamba, nazidalitsa, nanyema, napatsa ophunzira apereke kwa anthuwo.