Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 8:26 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anakocheza kudooko ku dziko la Agerasa, ndilo lopenyana ndi Galileya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo anakocheza kudooko ku dziko la Agerasa, ndilo lopenyana ndi Galileya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo adafika ku dziko la Ageregesa, limene lidapenyana ndi Galileya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anawolokera ku chigawo cha Gerasa chimene chili tsidya lina la nyanja kuchokera ku Galileya.

Onani mutuwo



Luka 8:26
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anati kwa iwo, Chikhulupiriro chanu chili kuti? Ndipo m'kuchita mantha anazizwa iwo, nanena wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti angolamula mphepo ndi madzi, ndipo zimvera Iye?


Ndipo atatuluka pamtunda Iye, anakomana naye mwamuna wa kumzinda, amene anali nazo ziwanda; ndipo masiku ambiri sanavale chovala, nisanakhala m'nyumba, koma m'manda.