Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 8:19 - Buku Lopatulika

Ndipo anadza kwa Iye amake ndi abale ake, ndipo sanakhoze kumfika, chifukwa cha khamu la anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anadza kwa Iye amake ndi abale ake, ndipo sanakhoze kumfika, chifukwa cha khamu la anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amai ake ndi abale ake a Yesu adabwera kunyumbako, koma chifukwa cha kuchuluka kwa anthu, adaalephera kufika pamene panali Iyepo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano amayi ndi abale a Yesu anabwera kudzamuona Iye, koma analephera kuti afike pafupi ndi Iye chifukwa cha gulu la anthu.

Onani mutuwo



Luka 8:19
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene abale ake anamva, anadza kudzamgwira Iye; pakuti anati adayaluka.


Ndipo anamuuza Iye, kuti, Amai wanu ndi abale anu alinkuima kunja, nafuna kuona Inu.