Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 8:11 - Buku Lopatulika

Koma fanizoli litere: Mbeuzo ndizo mau a Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma fanizoli litere: Mbeuzo ndizo mau a Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Tanthauzo la fanizoli ndi ili: Mbeu zija ndi mau a Mulungu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Tanthauzo la fanizoli ndi ili: Mbewu ndi mawu a Mulungu.

Onani mutuwo



Luka 8:11
10 Mawu Ofanana  

Kuchilamulo ndi kuumboni! Ngati iwo sanena malinga ndi mau awa, ndithu sadzaona mbandakucha.


Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.


Munthu aliyense wakumva mau a Ufumu, osawadziwitsai, woipayo angodza, nakwatula chofesedwacho mumtima mwake. Uyo ndiye wofesedwa m'mbali mwa njira.


Ndipo ananena nao, Simudziwa kodi fanizo ili? Mukazindikira bwanji mafanizo onse?


Ndipo za m'mbali mwa njira ndiwo anthu amene adamva; pamenepo akudza mdierekezi, nachotsa mau m'mitima yao, kuti angakhulupirire ndi kupulumuka.


Mwa ichi, mutavula chinyanso chonse ndi chisefukiro cha choipa, landirani ndi chifatso mau ookedwa mwa inu, okhoza kupulumutsa moyo wanu.