Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 7:48 - Buku Lopatulika

Ndipo anati kwa mkazi, Machimo ako akhululukidwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati kwa mkazi, Machimo ako akhululukidwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo Yesu adauza mai uja kuti, “Machimo ako akhululukidwa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anati kwa mayiyo, “Machimo ako akhululukidwa.”

Onani mutuwo



Luka 7:48
7 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, anabwera naye kwa Iye munthu wamanjenje, wakugona pamphasa: ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao, anati kwa wodwalayo, Limba mtima, mwana, machimo ako akhululukidwa.


Pakuti chapafupi nchiti, kunena, Machimo ako akhululukidwa; kapena kunena, Tanyamuka. Nuyende?


Ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao ananena ndi wodwala manjenje, Mwana, machimo ako akhululukidwa.


Chapafupi nchiti, kuuza wodwala manjenje kuti, Machimo ako akhululukidwa; kapena kuti, Nyamuka, senza mphasa yako, nuyende?


Ndipo Iye, pakuona chikhulupiriro chao, anati, Munthu iwe, machimo ako akhululukidwa.


Chapafupi nchiti, kunena, Akhululukidwa kwa iwe machimo ako; kapena kunena, Tauka, nuyende?


Chifukwa chake, ndinena kwa iwe, Machimo ake, ndiwo ambiri, akhululukidwa; chifukwa anakonda kwambiri; koma munthu amene anamkhululukira pang'ono, iye akonda pang'ono.