Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 7:23 - Buku Lopatulika

Ndipo wodala iye amene sakhumudwa chifukwa cha Ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo wodala iye amene sakhumudwa chifukwa cha Ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngwodala munthu amene sakhumudwa chifukwa cha Ine.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Odala munthu amene sakhumudwa chifukwa cha Ine.”

Onani mutuwo



Luka 7:23
11 Mawu Ofanana  

Ndipo wodala iye amene sakhumudwa chifukwa cha Ine.


Ndipo Simeoni anawadalitsa, nati kwa Maria amake, Taona, Uyu waikidwa akhale kugwa ndi kunyamuka kwa anthu ambiri mwa Israele; ndipo akhale chizindikiro chakutsutsana nacho;


Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Mukani, muuze Yohane zimene mwaziona, nimwazimva; anthu akhungu alandira kuona kwao, opunduka miyendo ayenda, akhate akonzedwa, ogontha akumva, akufa aukitsidwa, kwa aumphawi ulalikidwa Uthenga Wabwino.


Ndipo atachoka amithenga ake a Yohane, Iye anayamba kunena za Yohane kwa anthu a makamu aja, nati, Munatuluka kunka kuchipululu kukapenya chiyani? Bango logwedezeka ndi mphepo kodi?


Koma munthu wa chibadwidwe cha umunthu salandira za Mzimu wa Mulungu: pakuti aziyesa zopusa; ndipo sangathe kuzizindikira, chifukwa ziyesedwa mwauzimu.