Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 7:18 - Buku Lopatulika

Ndipo ophunzira a Yohane anamuuza iye zonsezi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ophunzira a Yohane anamuuza iye zonsezi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzira a Yohane adamsimbira zonsezi Yohaneyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ophunzira a Yohane anamuwuza Yohaneyo zinthu zonsezi. Atayitana awiri a ophunzirawo,

Onani mutuwo



Luka 7:18
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzira ake anadza, natola mtembo, nauika; ndipo anadza nauza Yesu.


Ndipo anadza kwa Yohane, nati kwa iye, Rabi, Iye amene anali ndi inu tsidya lija la Yordani, amene munamchitira umboni, taonani yemweyu abatiza, ndipo anthu onse alinkudza kwa Iye.