Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 7:15 - Buku Lopatulika

Ndipo wakufayo anakhala tsonga, nayamba kulankhula. Ndipo anampereka kwa amake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo wakufayo anakhala tsonga, nayamba kulankhula. Ndipo anampereka kwa amake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo wakufayo adakhala tsonga nayamba kulankhula, Yesu nkumupereka kwa mai wake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Wakufayo anakhala tsonga ndi kuyamba kuyankhula, ndipo Yesu anamupereka mnyamatayo kwa amayi ake.

Onani mutuwo



Luka 7:15
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu, pakuika maliro a munthu wina, anaona gulu la nkhondo, naponya mtembo m'manda mwa Elisa; koma pamene mtembowo unakhudza mafupa a Elisa, wakufayo anauka, naima chilili.


Nati, Katole. Natambasula dzanja lake, naitenga.


Ndipo anayandikira, nakhudza chithatha; ndipo akumnyamulawo anaima. Ndipo Iye anati, Mnyamata iwe, ndinena ndi iwe, Tauka.


Ndipo mantha anagwira onsewo: ndipo analemekeza Mulungu, nanena kuti, Mneneri wamkulu wauka mwa ife; ndipo Mulungu wadzacheza ndi anthu ake.