Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 7:10 - Buku Lopatulika

Ndipo pakubwera kunyumba otumidwawo, anapeza kapoloyo wachira ndithu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pakubwera kunyumba otumidwawo, anapeza kapoloyo wachira ndithu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Otumidwa aja adabwerera kunyumba, nakapeza wantchito uja atachiritsidwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anthu amene anatumidwawo anabwerera ku nyumba ndipo anakamupeza wantchitoyo atachira.

Onani mutuwo



Luka 7:10
6 Mawu Ofanana  

Pomwepo Yesu anayankha, nati kwa iye, Mkaziwe, chikhulupiriro chako ndi chachikulu; chikhale kwa iwe monga momwe wafunira. Ndipo mwana wake anachira nthawi yomweyo.


Ndipo Yesu anati kwa kenturiyoyo, Pita, kukhale kwa iwe monga unakhulupirira. Ndipo anachiritsidwa mnyamatayo nthawi yomweyo.


Ndipo Yesu ananena naye, Ngati mukhoza! Zinthu zonse zitheka ndi iye wakukhulupirira.


Ndipo kunali, katapita kamphindi, Iye anapita kumzinda, dzina lake Naini; ndipo ophunzira ake ndi mpingo waukulu wa anthu anapita naye.


Koma Yesu pakumva zimenezo anazizwa naye, napotolokera kwa anthu a mpingo wakumtsata Iye, nati, Ndinena kwa inu, sindinapeze, ngakhale mwa Israele, chikhulupiriro chachikulu chotere.