Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 5:31 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Amene ali olimba safuna sing'anga; koma akudwala ndiwo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Amene ali olimba safuna sing'anga; koma akudwala ndiwo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adaŵayankha kuti, “Anthu amene ali bwino sasoŵa sing'anga ai, koma amene akudwala.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anawayankha kuti, “Amene sakudwala safuna singʼanga, koma odwala.

Onani mutuwo



Luka 5:31
4 Mawu Ofanana  

Kodi mulibe vunguti mu Giliyadi? Kodi mulibe sing'anga m'menemo; analekeranji kuchira mwana wamkazi wa anthu anga?


Ndipo pamene Yesu anamva ichi, ananena nao, Akulimba safuna sing'anga, koma odwala ndiwo; sindinadza kudzaitana olungama, koma ochimwa.


Sindinadza Ine kuitana olungama, koma ochimwa kuti atembenuke mtima.