Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 4:44 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye analikulalikira m'masunagoge a ku Yudeya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye analikulalikira m'masunagoge a ku Yudeya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Iye ankalalika m'nyumba zamapemphero za ku Yudeya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Iye anapitirirabe kulalikira mʼmasunagoge a ku Yudeya.

Onani mutuwo



Luka 4:44
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anayendayenda mu Galileya monse, analikuphunzitsa m'masunagoge mwao, nalalikira Uthenga Wabwino wa Ufumu, nachiritsa nthenda zonse ndi kudwala konse mwa anthu.


Ndipo analowa m'masunagoge mwao mu Galileya monse, nalalikira, natulutsa ziwanda.


Ndipo Iye anaphunzitsa m'masunagoge mwao, nalemekezedwa ndi anthu onse.


Ndipo panali, pakumkanikiza khamu la anthu, kudzamva mau a Mulungu, Iye analikuimirira m'mbali mwa nyanja ya Genesarete;