Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 4:30 - Buku Lopatulika

Koma Iye anapyola pakati pao, nachokapo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Iye anapyola pakati pao, nachokapo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

koma Iye adangodzadutsa pakati pao, nkumapita.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Iye anangoyenda pakati pa gulu la anthulo nachokapo.

Onani mutuwo



Luka 4:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anatsika nadza ku Kapernao, ndiwo mzinda wa ku Galileya. Ndipo analikuwaphunzitsa iwo pa Sabata; ndipo anadabwa ndi chiphunzitso chake;


Anafunanso kumgwira Iye; ndipo anapulumuka m'dzanja lao.


Pamenepo anatola miyala kuti amponye Iye; koma Yesu anabisala, natuluka mu Kachisi.


Koma kutacha, panali phokoso lalikulu mwa asilikali, Petro wamuka kuti.