Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 4:19 - Buku Lopatulika

kulalikira chaka chosankhika cha Ambuye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kulalikira chaka chosankhika cha Ambuye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndi kukalalika za nthaŵi imene Ambuye adzapulumutsa anthu ao.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndi kulalikira za nthawi imene Ambuye adzakomere mtima anthu awo.”

Onani mutuwo



Luka 4:19
8 Mawu Ofanana  

Taona Mtumiki wanga, amene ndimgwiriziza; Wosankhika wanga, amene moyo wanga ukondwera naye; ndaika mzimu wanga pa Iye; Iye adzatulutsira amitundu chiweruziro.


ndikalalikire chaka chokomera Yehova, ndi tsiku lakubwezera la Mulungu wathu; ndikatonthoze mtima wa onse amene akulira maliro;


Pakuti tsiku lakubwezera lili mumtima mwanga, ndi chaka cha kuombola anthu anga chafika.


Ndipo pofika chaka choliza cha ana a Israele adzaphatikiza cholowa chao ku cholowa cha fuko limene akhalako; chotero adzachotsa cholowa chao ku cholowa cha fuko la makolo athu.


nanena, Ukadazindikira tsiku ili, inde iwetu zinthu za mtendere! Koma tsopano zibisika pamaso pako.


Ndipo ochita naye pamodzi tidandauliranso kuti musalandire chisomo cha Mulungu kwachabe inu,