Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 4:14 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu anabwera ndi mphamvu ya Mzimu ku Galileya; ndipo mbiri yake ya Iye inabuka ku dziko lonse loyandikira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu anabwera ndi mphamvu ya Mzimu ku Galileya; ndipo mbiri yake ya Iye inabuka ku dziko lonse loyandikira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adabwereranso ku Galileya ndi mphamvu za Mzimu Woyera. Mbiri yake idawanda kuzungulira dziko lonselo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anabwerera ku Galileya mu mphamvu ya Mzimu Woyera, ndipo mbiri yake inafalikira ku madera onse a ku midzi.

Onani mutuwo



Luka 4:14
10 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yesu anamva kuti anampereka Yohane, anamuka kulowa ku Galileya;


Ndipo mbiri yake imene inabuka m'dziko lonse limenelo.


Koma iwo anatulukamo, nabukitsa mbiri yake m'dziko lonselo.


Ndipo ataperekedwa Yohane, Yesu anadza ku Galileya, nalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu,


Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo.


Ndipo mdierekezi, m'mene adamaliza mayesero onse, analekana naye kufikira nthawi ina.


Ndipo mbiri yake ya Iye inafalikira kumalo onse a dziko loyandikira.


Koma atapita masiku awiriwo anachoka komweko kunka ku Galileya.


mauwo muwadziwa inu, adadzawo ku Yudeya lonse, akuyamba ku Galileya, ndi ubatizo umene Yohane anaulalikira;