Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 4:10 - Buku Lopatulika

pakuti kwalembedwa kuti, Adzalamula angelo ake za iwe, kuti akutchinjirize.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pakuti kwalembedwa kuti, Adzalamula angelo ake za iwe, kuti akutchinjirize.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Paja Malembo akuti, “ ‘Mulungu adzalamula angelo ake kuti akusamaleni.’ Ndiponso,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti kwalembedwa, “Adzalamulira angelo ake za iwe kuti akutchinjirize mosamala;

Onani mutuwo



Luka 4:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo, Pa manja ao adzakunyamula iwe, kuti ungagunde konse phazi lako pamwala.


Ndipo mdierekezi anati kwa Iye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, uzani mwala uwu usanduke mkate.


Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iye, Kwalembedwa, kuti, Ambuye Mulungu wako uzimgwadira, ndipo Iye yekhayekha uzimtumikira.


Ndipo kulibe kudabwa; pakuti Satana yemwe adzionetsa ngati mngelo wa kuunika.


Kodi siili yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa chipulumutso?