Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:8 - Buku Lopatulika

Ndipo anakumbukira mau ake,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anakumbukira mau ake,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo akazi aja adaŵakumbukiradi mauwo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anakumbukira mawu ake.

Onani mutuwo



Luka 24:8
4 Mawu Ofanana  

nabwera kuchokera kumanda, nafotokozera zonse khumi ndi mmodziwo, ndi otsala onse omwe.


Izi sanazidziwe ophunzira ake poyamba; koma pamene Yesu analemekezedwa, pamenepo anakumbukira kuti izi zinalembedwa za Iye, ndi kuti adamchitira Iye izi.


Koma Nkhosweyo, Mzimu Woyera, amene Atate adzamtuma m'dzina langa, Iyeyo adzaphunzitsa inu zonse, nadzakumbutsa inu zinthu zonse zimene ndinanena kwa inu.