Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:53 - Buku Lopatulika

ndipo anakhala chikhalire mu Kachisi, nalikuyamika Mulungu. Amen.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo anakhala chikhalire m'Kachisi, nalikuyamika Mulungu. Amen.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ankasonkhana m'Nyumba ya Mulungu nthaŵi ndi nthaŵi akutamanda Mulungu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo iwo anakhalabe ku Nyumba ya Mulungu, akulemekeza Mulungu.

Onani mutuwo



Luka 24:53
7 Mawu Ofanana  

ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


Ndipo iwowa anatuluka, nalalikira ponseponse, ndipo Ambuye anachita nao pamodzi, natsimikiza mau ndi zizindikiro zakutsatapo. Amen.


Ndipo anamlambira Iye, nabwera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu;


Pachiyambi panali Mau, ndipo Mau anali kwa Mulungu, ndipo Mau ndiye Mulungu.


Chisomo cha Ambuye Yesu chikhale ndi oyera mtima onse. Amen.