Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:52 - Buku Lopatulika

Ndipo anamlambira Iye, nabwera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamlambira Iye, nabwera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo adampembedza, pambuyo pake nkubwerera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo anamulambira Iye ndipo anabwerera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu.

Onani mutuwo



Luka 24:52
11 Mawu Ofanana  

Munasanduliza kulira kwanga kukhale kusekera; munandivula chiguduli changa, ndipo munandiveka chikondwero,


Ndipo pamene anamuona Iye, anamlambira; koma ena anakayika.


Ndipo onani, Yesu anakomana nao, nanena, Tikuoneni. Ndipo iwo anadza, namgwira Iye mapazi ake, namgwadira.


Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.


ndipo anakhala chikhalire mu Kachisi, nalikuyamika Mulungu. Amen.


Mwamva kuti Ine ndinanena kwa inu, Ndimuka, ndipo ndidza kwa inu. Mukadandikonda Ine, mukadakondwera kuti ndipita kwa Atate; pakuti Atate ali wamkulu ndi Ine.


Ndipo inu tsono muli nacho chisoni tsopano lino, koma ndidzakuonaninso, ndipo mtima wanu udzakondwera, ndipo palibe wina adzachotsa kwa inu chimwemwe chanu.


Koma ndinena Ine choonadi ndi inu; kuyenera kwa inu kuti ndichoke Ine; pakuti ngati sindichoka, Nkhosweyo sadzadza kwa inu; koma ngati ndipita ndidzamtuma Iye kwa inu.


Tomasi anayankha nati kwa Iye, Ambuye wanga, ndi Mulungu wanga.


Pamenepo anabwera ku Yerusalemu kuchokera kuphiri lonenedwa la Azitona, limene liyandikana ndi Yerusalemu, loyendako tsiku la Sabata.


amene mungakhale simunamuone mumkonda; amene mungakhale simumpenya tsopano, pokhulupirira, mukondwera naye ndi chimwemwe chosaneneka, ndi cha ulemerero: