Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:51 - Buku Lopatulika

Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akuŵadalitsa choncho, adalekana nawo, natengedwa kupita Kumwamba.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye akuwadalitsa, anawasiya ndipo anatengedwa kupita kumwamba.

Onani mutuwo



Luka 24:51
9 Mawu Ofanana  

Ndipo kunachitika, akali chiyendere ndi kukambirana, taonani, anaoneka galeta wamoto ndi akavalo amoto, nawalekanitsa awiriwa; Eliya nakwera kumwamba ndi kamvulumvulu.


Pamenepo Ambuye Yesu, atatha kulankhula nao, analandiridwa Kumwamba, nakhala padzanja lamanja la Mulungu.


Ndipo anatuluka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ake, nawadalitsa.


Ndipo anamlambira Iye, nabwera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu;


Yesu ananena naye, Usandikhudze, pakuti sinditha kukwera kwa Atate; koma pita kwa abale anga, ukati kwa iwo, Ndikwera kunka kwa Atate wanga, ndi Mulungu wanu.


Ndipo m'mene adanena izi, ali chipenyerere iwo, ananyamulidwa; ndipo mtambo unamlandira Iye kumchotsa kumaso kwao.


ameneyo, pokhala ali chinyezimiro cha ulemerero wake, ndi chizindikiro chenicheni cha chikhalidwe chake, nanyamula zonse ndi mau a mphamvu yake, m'mene adachita chiyeretso cha zoipa, anakhala padzanja lamanja la Ukulu mu Mwamba,


Popeza tsono tili naye Mkulu wa ansembe wamkulu, wopyoza miyamba, Yesu mwana wa Mulungu, tigwiritsitse chivomerezo chathu.