Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:34 - Buku Lopatulika

nanena, Ambuye anauka ndithu, naonekera kwa Simoni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nanena, Ambuye anauka ndithu, naonekera kwa Simoni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

akunena kuti, “Ambuye adaukadi, ndipo Simoni waŵaona.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo anati, “Ndi zoonadi! Ambuye auka ndipo anaonekera kwa Simoni.”

Onani mutuwo



Luka 24:34
7 Mawu Ofanana  

Koma mukani, uzani ophunzira ake, ndi Petro, kuti akutsogolerani inu ku Galileya; kumeneko mudzamuona Iye, monga ananena ndi inu.


Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso mu Galileya,


Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire.


Ndipo Yohane anaitana awiri a ophunzira ake, nawatuma kwa Ambuye, nanena, Kodi ndinu wakudzayo, kapena tiyang'anire wina?


kwa iwonso anadzionetsera yekha wamoyo ndi zitsimikizo zambiri, zitatha zowawa zake, naonekera kwa iwo masiku makumi anai, ndi kunena zinthu za Ufumu wa Mulungu;


ndi kuti anaonekera kwa Kefa; pamenepo kwa khumi ndi awiriwo;