Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:16 - Buku Lopatulika

Koma maso ao anagwidwa kuti asamzindikire Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma maso ao anagwidwa kuti asamzindikire Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma maso ao adaachita chidima, mwakuti sadamzindikire.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

koma iwo sanamuzindikire.

Onani mutuwo



Luka 24:16
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anazindikira abale ake, koma iwo sanamzindikire iye.


Ndipo zitatha izi, anaonekanso Iye m'maonekedwe ena kwa awiri a iwo alikuyenda kupita kumidzi.


Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao.


Ndipo anati kwa iwo, Mau awa ndi otani mulandizanawo poyendayenda? Ndipo anaima ndi nkhope zao zachisoni.


Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera.


M'mene adanena izi, anacheuka m'mbuyo, naona Yesu ali chilili, ndipo sanadziwe kuti ndiye Yesu.


Koma pakuyamba kucha, Yesu anaimirira pambali pa nyanja, komatu ophunzirawo sanadziwe kuti ndiye Yesu.