Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:12 - Buku Lopatulika

Koma Petro ananyamuka nathamangira kumanda, ndipo powerama anaona nsalu zabafuta pazokha; ndipo anachoka nanka kwao, nazizwa ndi chija chidachitikacho.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Petro ananyamuka nathamangira kumanda, ndipo powerama anaona nsalu zoyera pa zokha; ndipo anachoka nanka kwao, nazizwa ndi chija chidachitikacho.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe Petro adanyamuka nathamangira ku manda. Adaŵeramiramo naona nsalu zamaliro zokha, kenaka nkubwerera kunyumba akudabwa ndi zimene zidaachitikazo.]

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Komabe Petro anayimirira ndi kuthamangira ku manda. Atasuzumira, anaona nsalu zimene anamukulungira zija zili pa zokha, ndipo iye anachoka, akudabwa ndi zimene zinachitikazo.

Onani mutuwo



Luka 24:12
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo anatenga mtembo wa Yesu, nauzenenga ndi nsalu zabafuta pamodzi ndi zonunkhira, monga mwa maikidwe a maliro a Ayuda.