Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 23:6 - Buku Lopatulika

Koma pamene Pilato anamva, anafunsa ngati munthuyu ali Mgalileya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma pamene Pilato anamva, anafunsa ngati munthuyu ali Mgalileya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Pilato adamva zimenezi, adaŵafunsa kuti, “Kodi munthuyu ndi wa ku Galileya?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakumva zimenezi, Pilato anafunsa ngati munthuyo ndi Mgalileya.

Onani mutuwo



Luka 23:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Petro adakhala pabwalo: ndipo mdzakazi anadza kwa iye, nanena, Iwenso unali ndi Yesu wa ku Galileya.


Ndipo anakhalako nthawi yomweyo, anthu ena amene anamuuza Iye za Agalileya, amene Pilato anasakaniza mwazi wao ndi nsembe zao.


Koma iwo anapunda kunena kuti, Amautsa anthuwo, naphunzitsa mu Yudeya yense, kuyambira ku Galileya ndi kufikira kuno komwe.


Ndipo m'mene anadziwa kuti ali wa mu ulamuliro wake wa Herode, anamtumiza Iye kwa Herode, amene anali iye mwini ku Yerusalemu masiku awa.


Atapita ameneyo, anauka Yudasi wa ku Galileya, masiku a kalembera, nakopa anthu amtsate. Iyeyunso anaonongeka, ndi onse amene anamvera iye anabalalitsidwa.