Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 23:16 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake ndidzamkwapula ndi kummasula Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake ndidzamkwapula ndi kummasula Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero ndingomukwapula kenaka nkumumasula.” [

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼchifukwa chake, ine ndingomulanga, nʼkumumasula.”

Onani mutuwo



Luka 23:16
9 Mawu Ofanana  

Koma Iye analasidwa chifukwa cha zolakwa zathu, natundudzidwa chifukwa cha mphulupulu zathu; chilango chotitengera ife mtendere chinamgwera Iye; ndipo ndi mikwingwirima yake ife tachiritsidwa.


Pomwepo iye anamasulira iwo Barabasi, koma anakwapula Yesu, nampereka Iye kuti akampachike pamtanda.


Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.


Ndipo anati kwa iwo nthawi yachitatu, Nanga munthuyu anachita choipa chiyani? Sindinapeze chifukwa cha kufera Iye; chotero ndidzamkwapula Iye ndi kummasula.


Ndipo musawatsutsa, ndipo simudzamatsutsidwa. Khululukani, ndipo mudzakhululukidwa.


Koma Paulo anati kwa iwo, Adatikwapula ife pamaso pa anthu, osamva mlandu wathu, ife amene tili Aroma, natiika m'ndende; ndipo tsopano kodi afuna kutitulutsira ife m'tseri? Iai, ndithu; koma adze okha atitulutse.