Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 23:12 - Buku Lopatulika

Ndipo Herode ndi Pilato anachitana chibwenzi tsiku lomwelo; pakuti kale anadana.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Herode ndi Pilato anachitana chibwenzi tsiku lomwelo; pakuti kale anadana.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsiku lomwelo Herode ndi Pilato adayamba kuyanjana, chonsecho kale ankadana.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsiku limenelo, Herode ndi Pilato anakhala abwenzi. Zisanachitike izi anali adani.

Onani mutuwo



Luka 23:12
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi ndi Asaduki anadza, namuyesa, namfunsa Iye awaonetse chizindikiro cha Kumwamba.


ndipo anammanga Iye, namuka naye, nampereka Iye kwa Pilato kazembeyo.


Pakuti zoonadi anasonkhanidwa m'mzinda muno Herode, ndi Pontio Pilato yemwe pamodzi ndi amitundu ndi anthu a Israele kumchitira choipa Mwana wanu wopatulika Yesu amene munamdzoza;