Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 23:1 - Buku Lopatulika

Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Gulu lonse lija lidanyamuka nkupita naye Yesu kwa Pilato.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka gulu lonse la anthuwo linayimirira ndi kumutengera kwa Pilato.

Onani mutuwo



Luka 23:1
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene kunacha, bungwe la akulu a anthu linasonkhana, ndiwo ansembe aakulu ndi alembi; ndipo anapita naye kubwalo lao,


Ndipo iwo anati, Tifuniranjinso mboni? Pakuti ife tokha tinamva m'kamwa mwa Iye mwini.


Pakuti zoonadi anasonkhanidwa m'mzinda muno Herode, ndi Pontio Pilato yemwe pamodzi ndi amitundu ndi anthu a Israele kumchitira choipa Mwana wanu wopatulika Yesu amene munamdzoza;