Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:9 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo ananena naye, Mufuna tikakonzere kuti?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo ananena naye, Mufuna tikakonzere kuti?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma iwo adamufunsa kuti, “Kodi tikakonzere kuti?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anafunsa kuti, “Kodi mukufuna tikakonzere kuti?”

Onani mutuwo



Luka 22:9
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anayamba kulankhula nao m'mafanizo. Munthu analima munda wampesa, nauzunguniza ndi linga, nakumba moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Onani, mutalowa m'mzinda, adzakomana ndinu munthu alikusenza mtsuko wa madzi; mumtsate ameneyo kunyumba kumene akalowako iye.


Ndipo Iye anatumiza Petro ndi Yohane, nati, Pitani mutikonzere ife Paska, kuti tidye.