Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:71 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anati, Tifuniranjinso mboni? Pakuti ife tokha tinamva m'kamwa mwa Iye mwini.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo anati, Tifuniranjinso mboni? Pakuti ife tokha tinamva m'kamwa mwa Iye mwini.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo iwo aja adati, “Tikufuniranji umboni wina? Tadzimvera tokha mau akeŵa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo iwo anati, “Nanga tikufuniranjinso umboni wina? Ife tamva kuchokera pa milomo yake.”

Onani mutuwo



Luka 22:71
4 Mawu Ofanana  

Ndipo onse anati, Umo mtero, muli Mwana wa Mulungu kodi? Ndipo Iye anati kwa iwo, Munena kuti ndine.


Ndipo khamu lonselo linanyamuka kupita naye kwa Pilato.