Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:68 - Buku Lopatulika

ndipo ndikakufunsani kanthu, simudzayankha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo ndikakufunsani kanthu, simudzayankha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo nditakufunsani funso, inu simungaliyankhe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine nditakufunsani inu, simungandiyankhe.

Onani mutuwo



Luka 22:68
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yeremiya anati kwa Zedekiya, Ndikakufotokozerani, kodi simudzandipha ine? Ndipo ndikakupangirani, simudzandimvera ine.


nanena, Ngati uli Khristu, utiuze. Ndipo anati kwa iwo, Ndikakuuzani, simudzavomereza;


Koma kuyambira tsopano Mwana wa Munthu adzakhala padzanja lamanja la mphamvu ya Mulungu.