Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:6 - Buku Lopatulika

Ndipo iye anavomera, nafunafuna nthawi yabwino yakumpereka Iye kwa iwo, pakalibe khamu la anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iye anavomera, nafunafuna nthawi yabwino yakumpereka Iye kwa iwo, pakalibe khamu la anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yudasi adavomera, nayamba kufunafuna mpata woti amuperekere kwa iwo, anthu onse osadziŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anavomera, ndipo anayamba kufunafuna mpata wabwino wakuti amupereke Yesu kwa iwo pamene panalibe gulu la anthu pafupi.

Onani mutuwo



Luka 22:6
4 Mawu Ofanana  

Koma ananena iwo, pa nthawi ya chikondwerero iai, kuti pasakhale phokoso la anthu.


pakuti anati, Pachikondwerero ai, kuti pangakhale phokoso la anthu.


Ndipo anakondwera, napangana naye kumpatsa ndalama.


Ndipo tsiku la mikate yopanda chotupitsa linafika, limene inayenera kuphedwa nsembe ya Paska.