Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:57 - Buku Lopatulika

Koma anakana, nati, Mkaziwe, sindimdziwa Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma anakana, nati, Mkaziwe, sindimdziwa Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Petro adakana, adati, “Mai iwe, sindimdziŵa ameneyu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Petro anakana nati, “Mtsikana, ine sindimudziwa ameneyu.”

Onani mutuwo



Luka 22:57
12 Mawu Ofanana  

Koma yense amene adzandikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamkana iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba.


Koma iye anakana pamaso pa anthu onse, kuti, Chimene unena sindichidziwa.


Koma iye wondikana Ine pamaso pa anthu, iye adzakanidwa pamaso pa angelo a Mulungu.


Ndipo mdzakazi anamuona iye alikukhala m'kuwala kwake kwa moto, nampenyetsa iye, nati, Munthu uyunso anali naye.


Ndipo popita kamphindi, anamuona wina, nati, Iwenso uli mmodzi wa awo. Koma Petro anati, Munthu iwe, sindine.


Koma Simoni Petro analikuimirira ndi kuotha moto. Pomwepo anati kwa iye, Suli iwenso wa ophunzira ake kodi? Iyeyu anakana, nati, Sindine.


Pamenepo Petro anakananso; ndipo pomwepo analira tambala.


Chifukwa chake lapani, bwererani kuti afafanizidwe machimo anu, kotero kuti zidze nyengo zakutsitsimutsa zochokera kunkhope ya Ambuye;


Ngati tivomereza machimo athu, ali wokhulupirika ndi wolungama Iye, kuti atikhululukire machimo athu, ndi kutisambitsa kutichotsera chosalungama chilichonse.