Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:23 - Buku Lopatulika

Ndipo anayamba kufunsana mwa iwo okha, ndiye yani mwa iwo amene adzachita ichi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anayamba kufunsana mwa iwo okha, ndiye yani mwa iwo amene adzachita ichi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo onse adayamba kumafunsana kuti, “Kodi ndani mwa ife angachite zotere?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anayamba kufunsana pakati pawo kuti ndi ndani wa iwo amene akanachita ichi.

Onani mutuwo



Luka 22:23
5 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anagwidwa ndi chisoni chachikulu, nayamba kunena kwa Iye mmodzimmodzi, Kodi ndine, Ambuye?


Anayamba iwo kukhala ndi chisoni, ndi kunena naye mmodzimmodzi, kuti, Ndine kodi?


Pakuti Mwana wa Munthu amukatu, monga kunaikidwiratu; koma tsoka munthuyo amene ampereka!


Ndipo kunakhala kutsutsana mwa iwo, ndani wa iwo ayesedwe wamkulu.