Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:21 - Buku Lopatulika

Koma onani, dzanja lake la iye amene adzandipereka ali pagome pano pamodzi ndi Ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma onani, dzanja lake la iye amene adzandipereka ali pagome pano pamodzi ndi Ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Koma ndithudi wondipereka kwa adani akudya nane pamodzi pompano.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma dzanja la amene akundipereka Ine lili pamodzi ndi langa pa chakudya pano.

Onani mutuwo



Luka 22:21
9 Mawu Ofanana  

mabwenzi anga enieni onse anyansidwa nane; ndi onse ndakondana nao asandulika adani anga.


Ngakhale bwenzi langa lenileni, amene ndamkhulupirira, ndiye amene adadyako mkate wanga, anandikwezera chidendene chake.


Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.


Ndipo Yesu anayankha, Ndi iyeyu, amene Ine ndidzamsunsira nthongo ndi kumpatsa. Pamenepo, m'mene anasunsa nthongo anaitenga naipatsa Yudasi mwana wa Simoni Iskariote.