Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:14 - Buku Lopatulika

Ndipo itadza nthawi yake, Iye anakhala pachakudya, ndi ophunzira pamodzi ndi Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo itadza nthawi yake, Iye anakhala pachakudya, ndi ophunzira pamodzi ndi Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵi itakwana, Yesu adakakhala podyera pamodzi ndi atumwi ake aja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ora litakwana, Yesu ndi ophunzira ake anakhala pa tebulo.

Onani mutuwo



Luka 22:14
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pakufika madzulo, Iye analinkukhala pachakudya pamodzi ndi ophunzira khumi ndi awiri;


Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.


Ndipo atumwi anasonkhana kwa Yesu; namuuza zilizonse adazichita, ndi zonse adaziphunzitsa.


Ndipo anapita iwo, napeza monga adatero nao; ndipo anakonza Paska.


Ndipo anati kwa iwo, Ndinalakalaka ndithu kudya Paska uwu pamodzi ndinu, ndisanayambe kusautsidwa;