Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 22:13 - Buku Lopatulika

Ndipo anapita iwo, napeza monga adatero nao; ndipo anakonza Paska.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapita iwo, napeza monga adatero nao; ndipo anakonza Paska.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono iwo adapita nakachipezadi monga momwe adaaŵauzira, ndipo adakonza phwando la Paska.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anapita nakapeza zinthu monga mmene Yesu anawawuzira. Tsono anakonza Paska.

Onani mutuwo



Luka 22:13
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anachoka otumidwawo, napeza monga adanena kwa iwo.


Thambo ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.


Ndipo iyeyo adzakuonetsani chipinda chachikulu chapamwamba, chokonzeka; mukakonzere kumeneko.


Ndipo itadza nthawi yake, Iye anakhala pachakudya, ndi ophunzira pamodzi ndi Iye.


Yesu ananena naye, Kodi sindinati kwa iwe, kuti, ngati ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu?


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.


Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.