Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 20:4 - Buku Lopatulika

Ubatizo wa Yohane unachokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ubatizo wa Yohane unachokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

kodi Yohane Mbatizi kuti azibatiza, mphamvu zake adaazitenga kwa yani, kwa Mulungu kapena kwa anthu?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

‘Kodi ubatizo wa Yohane, unali wochokera kumwamba, kapena wochokera kwa anthu?’ ”

Onani mutuwo



Luka 20:4
10 Mawu Ofanana  

Ndidzanyamuka ndipite kwa atate wanga, ndipo ndidzanena naye, Atate, ndinachimwira Kumwamba ndi pamaso panu;


Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Ndidzakufunsani mau Inenso; mundiuze:


Ndipo anatsutsana mwa okha, nanena, Ngati tinena uchokera Kumwamba; adzati, Simunamkhulupirire chifukwa ninji?


Kunali munthu, wotumidwa ndi Mulungu, dzina lake ndiye Yohane.