Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 20:12 - Buku Lopatulika

Ndipo anatumizanso wina wachitatu; ndipo iyenso anamlasa, namtaya kunja.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatumizanso wina wachitatu; ndipo iyenso anamlasa, namtaya kunja.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adatumanso wachitatu, koma uyunso alimiwo adamuvulaza, namtaya kunja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anatumizanso wina wachitatu ndipo iwo anamuvulaza namuponya kunja.

Onani mutuwo



Luka 20:12
3 Mawu Ofanana  

Pomwepo anati kwa wina, Ndipo iwe uli nao mangawa otani? Ndipo uyu anati, Madengu a tirigu zana. Iye ananena naye, Tenga kalata yako nulembere makumi asanu ndi atatu.


Ndipo anatumizanso kapolo wina; ndipo iyenso anampanda, namchitira chipongwe, nambweza, wopanda kanthu.


Ndipo mwini mundawo anati, Ndidzachita chiyani? Ndidzatuma mwana wanga amene ndikondana naye; kapena akamchitira iye ulemu.