Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 2:50 - Buku Lopatulika

Ndipo sanadziwitse mau amene Iye analankhula nao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo sanadziwitse mau amene Iye analankhula nao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma iwo sadamvetse zimene adaŵayankhazo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma iwo sanazindikire chomwe Iye amatanthauza.

Onani mutuwo



Luka 2:50
3 Mawu Ofanana  

Koma iwo sanazindikire mauwo, naopa kumfunsa.


Ndipo sanadziwitse kanthu ka izi; ndi mau awa adawabisikira, ndipo sanazindikire zonenedwazo.


Koma iwo sanadziwitse mau awa, ndipo anabisidwa kwa iwo, kuti asawadziwe; ndipo anaopa kumfunsa za mau awa.