Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 2:45 - Buku Lopatulika

ndipo pamene sanampeze, anabwera ku Yerusalemu, namfunafuna Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo pamene sanampeze, anabwera ku Yerusalemu, namfunafuna Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ataona kuti sakumpeza, adabwerera ku Yerusalemu akumufunafuna ndithu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atalephera kumupeza, anabwerera ku Yerusalemu kukamufuna.

Onani mutuwo



Luka 2:45
2 Mawu Ofanana  

koma iwo anayesa kuti Iye ali m'chipiringu cha ulendo, nayenda ulendo wa tsiku limodzi; ndipo anayamba kumfunafuna Iye mwa abale ao ndi mwa anansi ao;


Ndipo pakupita masiku atatu, anampeza Iye mu Kachisi, analikukhala pakati pa aphunzitsi, namva iwo, nawafunsanso mafunso.