Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 2:42 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene Iye anakhala ndi zaka zake khumi ndi ziwiri, anakwera iwo monga machitidwe a chikondwerero;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene Iye anakhala ndi zaka zake khumi ndi ziwiri, anakwera iwo monga machitidwe a chikondwerero;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Yesu anali ndi zaka khumi ndi ziŵiri, iwo adapita kumeneko monga adaazoloŵera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye ali ndi zaka khumi ndi ziwiri, anapita ku phwando, monga mwa mwambo.

Onani mutuwo



Luka 2:42
5 Mawu Ofanana  

Katatu m'chaka amuna onse azioneka pamaso pa Ambuye Yehova.


Ndipo atate wake ndi amake akamuka chaka ndi chaka ku Yerusalemu ku Paska.


ndipo pakumaliza masiku ake, pakubwera iwo, mnyamatayo Yesu anatsala m'mbuyo ku Yerusalemu. Ndipo atate ndi amake sanadziwe;


Ndipo anadza ku Nazarete, kumene analeredwa; ndipo tsiku la Sabata analowa m'sunagoge, monga anazolowera, naimiriramo kuwerenga m'kalata.


Chifukwa chake pamene anadza ku Galileya, Agalileya anamlandira Iye, atakaona zonse zimene anazichita mu Yerusalemu pachikondwerero; pakuti iwonso ananka kuchikondwerero.