Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 2:30 - Buku Lopatulika

chifukwa maso anga adaona chipulumutso chanu,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chifukwa maso anga adaona chipulumutso chanu,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndi maso angaŵa ndachiwonadi chipulumutso chija,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti maso anga aona chipulumutso chanu,

Onani mutuwo



Luka 2:30
11 Mawu Ofanana  

Ndadikira chipulumutso chanu, Yehova.


Ndinayembekeza chipulumutso chanu, Yehova, ndipo ndinachita malamulo anu.


Ndinakhumba chipulumutso chanu, Yehova; ndipo chilamulo chanu ndicho chondikondweretsa.


inde, ati, Chili chinthu chopepuka ndithu kuti Iwe ukhale mtumiki wanga wakuutsa mafuko a Yakobo, ndi kubwezera osungika a Israele; ndidzakupatsanso ukhale kuunika kwa amitundu, kuti ukhale chipulumutso changa mpaka ku malekezero a dziko lapansi.


Yehova wavula mkono wake woyera pamaso pa amitundu onse; ndi malekezero onse a dziko lapansi adzaona chipulumutso cha Mulungu wathu.


chimene munakonza pamaso pa anthu onse,


ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.


Potero, dziwani inu, kuti chipulumutso ichi cha Mulungu chitumidwa kwa amitundu; iwonso adzamva.